WAGWIDA POFUNA KUDETSA DZINA LA CHILIMA KALIKONSE MUKAONA
Pamene anthu mdziko muno ali kukumana ndi mavuto osiyanasiyana kamba kakusowa luntha ndi utsogoleri wa Tonse Alliance womwe ukutsogoleredwa ndi chipani cha Malawi Congress (MCP) ndi mtsogoleri wake a Lazarus Chakwera, pali anthu ena omwe akumatuma atolankhani mdziko muno kuti adzilemba nkhani zonyazitsa wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima
Ещё видео!